1.
Mlungu dalitsani Malawi,
Mumsunge m'mtendere.
Gonjetsani adani onse,
Njala, nthenda, nsanje.
Lunzitsani mitima yathu,
Kuti tisaope.
Mdalitse Mtsogo leri na fe,
Ndi Mai Malawi.
2.
Malawi ndziko lokongola,
La chonde ndi ufulu,
Nyanja ndi mphepo ya m'mapiri,
Ndithudi tadala.
Zigwa, mapiri, nthaka, dzinthu,
Find More lyrics at www.sweetslyrics.com
N'mphatso zaulere.
Nkhalango, madambo abwino.
Ngwokoma Malawi.
3.
O! Ufulu tigwirizane,
Kukweza Malawi.
Ndi chikondi, khama, kumvera,
Timutumikire.
Pa nkhondo nkana pa mtendere,
Cholinga n'chimodzi.
Mai, bambo, tidzipereke,
Pokweza Malawi.
Sent by Carlos André Pereira da Silva Branco
Most searched Unknown lyrics :1) I Have A Father Who Can 2) 99 Bottles Of Beer On The Wall 3) Thank You Once Again 4) Shooting Star 5) Feeling my Swagger 6) Like a horcrux 7) A Plea For One World 8) Adore You 9) Kære Linedanser (dansk) 10) Albania Anthem Native Text
Malawi Native Anthem Text lyrics @ elyricsworld.com
